Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 107
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 107

Nyimbo 107

Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!

(2 Mbiri 20:21)

1. Titame Yehova molimbika,

M’nyonga yake timenya nkhondo.

Mdani asatiwopseze konse.

Musawawope, tiyenitu.

(Korasi)

2. Titame Yehova molimbika

Tichenjeze onse mokweza;

Kuti Mfumu idzatha oipa,

Inde nthaŵi yayandikira.

(Korasi)

3. Titame Yehova molimbika,

Pophunzitsa owona mtima,

Kuwasonyeza mwaŵi wantchito,

Ofuna kuchita za M’lungu.

(KORASi)

Lengeza chipulumutso chake.

Thandiza anthu kudzipereka.

Titame Yehova molimbika,

Kwezani dzina loyeralo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena