Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 146
  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Thawirani ku Ufumu wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 146

Nyimbo 146

Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!

(Zefaniya 2:3)

1. Funani Yehova inu ofatsa;

Chilungamo ndi kufatsa lero.

Potero pena mutsiku lamkwiyo

Kuti mudzabisikadi.

(Korasi)

2. Inu anjalatu ya chowonadi;

Bwanji mufu’la mowawa mtima?

Funani njira kuthaŵa opsinja,

Gonjani kwa Kristu Mfumu.

(Korasi)

3. Kwezani mitu, E, mosangalala.

Zitsimikizo za Ufumuwo!

Chingamira kuŵala kwa Yehova,

Muwopeni iye yekha!

(KORASi)

Thaŵirani ku Ufumu wake;

Imani molimbika. (molimba.)

Kumeneko mudzabisikakodi;

Kangazani kumumva. (kumumva.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena