Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 142
  • Chiyembekezo cha Chilengedwe cha Chimasuko

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chiyembekezo cha Chilengedwe cha Chimasuko
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
    Imbirani Yehova
  • Bwerani Mudzalimbikitsidwe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalidwe la Ubwino
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 142

Nyimbo 142

Chiyembekezo cha Chilengedwe cha Chimasuko

(Aroma 8:21)

1. Chilengedwe chonse chivutika;

Chituta zofesa zake.

Chakana M’lungu; Chikugonjera

Kuzinthu zovulazadi.

2. Poyembekeza chipulumutso,

Anthu ayang’ane kwa Ya.

Ngwokoma mtima, athandizadi

Kwa onse obuulawo.

3. Kuchimasuko ndi kubwezera

Anthuwo adzapezadi.

Mwana wa M’lungu, wasankhidwadi

Kuti anthu ayanjidwe.

4. Kugwirizana ndi “mtundu” wa Ya

Kumadzetsa madalitso.

Adikilira, nayembekeza,

Kukondwera ndi Ufumu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena