Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 125
  • ‘Yehova Ali Kumbali Yanga’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Yehova Ali Kumbali Yanga’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imani ndi Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 125

Nyimbo 125

‘Yehova Ali Kumbali Yanga’

(Salmo 118:6)

1. Mtima wanga pa Yehova

Udalira kwambiri.

Ndikhumba kuyenda naye

Ndi kumumamatira.

Munjirayo mungakhale

Mikhalidwe yovuta,

Koma M’lungu ali nane.

Mtima wanga ukondwa!

(Korasi)

2. Ndidziŵa munthaŵi ino Kuti ndidzayesedwa.

Mdani ndi ziwanda zake

Afunatu kundipha.

Koma ndingawapambane,

Mwachithandizo cha Ya.

Okhala ndi dzina lake

Mulungu awakonda.

(Korasi)

3. Yehova wakulitsadi

Mtundu wake woyera.

Ambiri adza nasunga

Malamulo akewo.

Achirikiza onsewo;

Mwa iwo akondwera.

Nanenso ndichite changu

Kumlingo waukulu.

(KORASI)

Ya ali kumbali yanga;

Ndidzamutamanda kosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena