Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 15
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 15

Nyimbo 15

Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!

(Yohane 3:16)

1. Kodidi mungawone,

Anthu ali pamodzi?

Chisonicho Chathadi!

Mtendere wadzadi.

(Korasi)

2. Anthu ndi nyama ali

Pamodzi mumtendere.

Chakudyanso Chiripo

Chopatsidwa ndi Ya.

(Korasi)

3. M’nthaŵiyo nkhalambadi,

Khungu lidzasalala.

Mavutowo, Athadi

Sitimawopanso.

(Korasi)

4. Onsewo adzakondwa

Poimbira Mulungu.

Nthaŵi zonse tidzati

“Zikomo” kwa M’lungu!

(KORASi)

Imbani mokondwa.

Mungagaŵanemo.

Panthaŵiyo mudzati:

“Moyo wamuyaya!”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena