Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 96
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kugonjetsa Dziko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kupeza Ubwenzi wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamani Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 96

Nyimbo 96

Kulemekeza Atate Wathu Yehova

(Yohane 17:4)

1. Ya chilengedwe chiimba

Za mphamvu ndi ulemu.

Ndi chifuno zolengedwa

Zanu zinakhalapo.

Mupereka madalitso,

Ndi mphatso zabwinonso.

Mwachititsa ulosiwo

Kukwaniritsidwadi.

Pobadwa Yesu angelo

Anamulemekeza.

Kupyola mwa Mbuye Kristu,

Mwaperekatu dipo!

2. Tidziŵatu Mwana wanu

Anakwanitsa ntchito,

Analilaka dzikoli

Nasintha makhalidwe,

Monga Mfumu pachimpando

Apatsa malamulo,

Adziŵitsatu dzinalo

Kumitundu yadziko,

Eya tipeza chimwemwe

Pakuimbira inu:

‘Mbuye Ya wa kuunika,

Adzachotsa chisoni.’

3. Kodi tingamuimbire,

Ndi kumusangalatsa?

Tichite kudzipereka,

Ndi kumutumikira?

Tigwiritsitse dzinalo,

Ntchito itsirizidwe.

Chikondi chisazirale,

Changu chathu chisathe.

Koma ndi mitima yathu

Tikutumikirani.

Kulemekeza dzinalo

Tidzayesa kutero.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena