Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 220
  • Paradaiso Wathu: Tsopano ndi Mtsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Paradaiso Wathu: Tsopano ndi Mtsogolo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova, Malo Athu Okhalamo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova, Mlengi Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kudzisungira Ife Eni Monga “Wamng’ono”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 220

Nyimbo 220

Paradaiso Wathu: Tsopano ndi Mtsogolo

(2 Akorinto 12:4)

1. Titamanda Yehova M’lungu

Ka’mba ka paradaiso,

Pophunzira ndi posonkhana

Timakhala anzeru.

Tiyamikiretu

Madalitsowo

Tisangalalatu

Ndi ntchito yanu!

Chikondi chanu ndi cha mnansi

Nchomangira cholimba.

Chitigwirizanitsa m’ntchito,

Kuti ife tisagwe!

2. Kulamulira kolungama

Mwapatsa Kristu Mfumu.

Padzanja lanu lamanjalo

Alamula ponsepo.

Titama Yehova,

Potidziŵitsa

Chifuniro chanu

Chosonkhanitsa.

Khalidwe lathu likhalebe

Loyenera mbiriyo,

Kuti tisakhumudwitsetu

Anthu onga nkhosawo!

3. Nkhondo yaikulu itatha

Yomenyedwa ndi M’lungu,

Satana ndi ziwanda zake

Ataponyedwa m’phompho,

Atumiki anu Adzaukadi,

Kudzatumikira

Mu Paradaiso.

Anthu adzakhala angwiro

Kupyolera munsembe;

Ndiyeno padziko kosatha,

Padzakhala chimwemwe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena