Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 144
  • Tiyenera Kukhala ndi Chikhulupiliro

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyenera Kukhala ndi Chikhulupiliro
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 144

Nyimbo 144

Tiyenera Kukhala ndi Chikhulupiliro

(Ahebri 10:39)

1. Nthaŵi zakale M’lungu ananena

Kupyolera mwa aneneri ake.

Koma tsono wanena mwa Mwana’ke;

Mwa kumvetsera tidzapulumuka.

(Korasi)

2. Tisataye ufulu wa kunena,

Tikhale olimba polalikira.

Tikatsanza chitsanzo cha Ambuye,

Yehova adzatifupadi ife.

(Korasi)

3. Sitidzabwerera kuchitayiko,

Komatu tiri okhulupirika.

Nkana adaniwo akutizinga,

Tidzakhulupilirabe Yehova.

(KORASI)

Tikhulupiriretu mu Baibulo.

Kuti tipulumuke nkhondo ya M’lungu.

Tiri ndi chikhulupiro cha ntchito?

Nchimenecho tidzapulumuka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena