Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 195
  • Iri Nditsiku la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Iri Nditsiku la Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ndipo Adzadziŵa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 195

Nyimbo 195

Iri Nditsiku la Yehova

(Salmo 118:24)

1. Tsiku nla Yehova. Kulamula nkwake.

Waikatu mu Ziyoni mwala.

Kwezanidi mawu Kuyamika M’lungu,

Poti mwa Yehova timakhulupira.

(Korasi)

2. Kristu alamula, Mapeto afika.

Dziko la Satana likupita.

Lalikira Mawu; Thandiza ofatsa

Kumveratu malamulo a Mulungu.

(Korasi)

3. Titama Mfumuyo; Imatidabwitsa.

Ikudza mudzina la Mulungu.

Loŵa pazipata! O tiyanjidwetu

Kuti tikhalebe mu’tumiki wake.

(KORASi)

Udzetsanji, Ufumu wa Ya?

Chilakiko cha Cho’nadi.

Nchiyaninso, Ufumu wa Ya?

Moyo wosatha m’chimwemwe.

Tamani Mfumu Yosatha

Ka’mba ka chikondicho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena