Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 225
  • Kuyandikira kwa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyandikira kwa Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Kuyandikira kwa Mulungu Ndi Chinthu Chabwino” kwa Ife
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Yehova Ndiye Chitsanzo Chachikulu Pankhani Yosonyeza Ubwino
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Mbali Yodabwitsa ya Ubwino wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1989
  • “Ubwino Wake Ndi Waukulu Kwambiri!”
    Yandikirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 225

Nyimbo 225

Kuyandikira kwa Yehova

(Salmo 73:28)

1. Chiyanjo chanu O Ya,

Ndichodalirika.

Monga odzipereka,

Tiyandikira’nu.

Ndi chuma chapatali

Ngati muli bwenzi.

Chikondi chanu nchoyera.

Tikuyamikani.

2. Ndinu Mbusa wamkulu,

Mutisamalira

Mwa Kristu mwatidzetsa,

Talisiya dziko.

Mwatikhululukira

Mwachifundo chanu.

Ndinu wabwino; tikondwa

Pokhala ndi inu.

3. Tinaphunzira zanu

Ndi kukutamani.

Chikondi ndi ukoma,

Zimatidabwitsa.

Tifuna kudziŵanu,

Ndi kuyandikabe.

Mutichitire mokoma;

Tichite chifuno.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena