Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 61
  • “Ndine Yehova”!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndine Yehova”!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ndipo Adzadziŵa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 61

Nyimbo 61

“Ndine Yehova”!

(Yesaya 42:8)

1. Imvani mafumu a dziko

Anyalanyazadi Yehova.

Sasankha kuvomereza ufumu,

Ndipo anyoza mphamvu yake.

Kodi ndani anagwetsa magulu,

Nawonongedwadi mwamanyazi?

Indedi ndani anatontholetsa

Ndi kupatsa anthu chipambano?

(Korasi)

2. Mafumu a dziko amvana

Mukutsutsana ndi Mwanayo!

Koma amphamvuwo ali ndi mantha,

Pomwe amphaŵi abuula.

Kodi ndani adzathyola golilo

Napulumutsa ofatsa m’dziko?

Ndani adzasandutsa chilungamo

Chisoni nachikhala chimwemwe?

(KORASI)

Ndine Mbuye; palibe wina.

Ndine Mbuye; Ndinedi Yehova.

Ndakhazika Mfumu yanga paphiri;

Mgwadireni! Yesu alamula.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena