Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 135
  • Yehova, Malo Athu Okhalamo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Malo Athu Okhalamo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amatidziŵitsa Kuŵerenga Masiku Athu
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Paradaiso Wathu: Tsopano ndi Mtsogolo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Ndi Malo Athu Okhalamo
    Nsanja ya Olonda—2013
  • “Akunga Yehova Mulungu Wathu Ndani?”
    Nsanja ya Olonda—1992
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 135

Nyimbo 135

Yehova, Malo Athu Okhalamo

(Salmo 90:1)

1. Ya malo athu okhalamo

Mumibadwo yathu yonse.

Musanapangetu mapiri,

Inu munalipo kale.

Ndinu M’lungu wanthaŵi zonse;

Kuzaka zosatha konse.

Chinkana tiri ngati ‘fumbi,’

Munatikonda kwambiri.

2. Zaka chikwi kwa inu ziri

Ngati dzulo lapitali.

Munthu afanana ndi msipu

Aphukira ndi kufota.

Tikhala makumi asanu

N’aŵiri pena atatu;

Koma zaka zathu nzovuta,

Zodzazidwa ndi chisoni.

3. Mutiphunzitse kuŵerenga

Masiku tisangalale.

Mitima ikhale ndi nzeru,

Milomo itamandenu.

Yehova khalani wokondwa

Po’na atumiki anu.

Limbikitsani ntchito yathu;

Manja athu mulimbitse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena