Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 169
  • Nyimbo Yatsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo Yatsopano
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 169

Nyimbo 169

Nyimbo Yatsopano

(Salmo 98:1)

1. Imba kwa Mbuye nyimbo yachikondwelero;

Ya zinthu wachita ndi za kudzachita.

Tama mkonowo, ndi dzanja lake lamanja;

Waweruza anthu onse molungama.

(Korasi)

2. Fu’la mokondwa kwa Yehova dziko lonse;

Imbani kwa M’lungu zitamando zanu.

Tama Yehova, imbani pamaso pake,

Zoimbira zonse zigwirizanedi.

(Korasi)

3. Nyanja yamphamvu zonse za m’mwemo zibume,

Okhala padziko aimbe mokondwa.

Madzi akondwe mitsinje isangalale,

Mitunda nayonso iimbe ponsepo.

(KORASI)

Imbani!

Nyimbo Yatsopano.

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena