Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 175
  • Miyamba Imalengeza Ulemelero wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Miyamba Imalengeza Ulemelero wa Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Zakumwamba Zimalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Kumwamba Kumalengeza Ulemerero wa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Zikumbutso za Yehova Mumazikonda Kwambiri?
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 175

Nyimbo 175

Miyamba Imalengeza Ulemelero wa Mulungu

(Salmo 19:1)

1. Miyamba ilengeza za Yehova;

Tiziwona ntchito zake mlengalenga.

Usana umtamandadi;

Usiku usonyezatu mphamvu yake.

2. Lamulo la Yehova ndi langwiro,

Malangizo ake achititsa nzeru.

Ndipo malamulo ake;

Asangalatsa mtima ndi maso athu.

3. Kuwopa Yehova kuli kwanzeru.

Ziweruzo zake ziri zolungama

Ndi zofunika kwambiri,

Zosangalatsa pakudya, ngati uchi.

4. Tiyamika ka’mba ka malamulo;

Tidzapeza mphotho ngati tiwasunga.

Mumaganizo ndi mawu

Zipezedwe zowonadi, ’mbuye Mfumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena