Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 13
  • Kudzipatulira Kwachikristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzipatulira Kwachikristu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tidzipereke Monga Akhristu
    Imbirani Yehova
  • Kudzipereka Monga Mkhristu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Odzipatulira—Kwa Yani?
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Anabadwira mu Mtundu Wosankhika wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 13

Nyimbo 13

Kudzipatulira Kwachikristu

(Eksodo 39:30)

1. Chifukwa Ya analenga

Chilengedwe chonse,

Dziko ndi miyamba nzake,

Ziri ntchito zake.

Wapatsa mpweya wa moyo

Nasonyeza kuti

Ngwoyenera kutamandidwa,

Kulambiranso nkwake.

2. Pa Sinai Israyeli

Wakale anati:

Tidzasunga Lamulo la

Yehova mokondwa.

Anali mwamuna wawo;

Powagula m’nyanja.

Mtundu wa odziperekawo

Mwenzi ukadatero.

3. Yesu anabatizidwa

Ka’mba ka Ubwino,

Nadzipereka kuchita

Chifuno cha M’lungu.

Atatuluka m’Yordano

Monga wodzozedwa,

Kuti atumikire monga

Wopatulika wa Ya.

4. Tidza kwa inu Yehova,

Kudzakutamani.

Modzichepetsa mtimatu

Tikudzipereka.

Munatipatsa Mwanayo,

Napereka mtengo.

Sitidzadzikhalira moyo,

Koma ka’mba ka inu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena