Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 222
  • Yang’ananibe Maso Anu Pamphotho!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yang’ananibe Maso Anu Pamphotho!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yang’ananibe Pamphotho!
    Imbirani Yehova
  • Mukhulupirikebe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Musalole Kuti Chilichonse Chikulepheretseni Kulandira Mphoto
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Yang’ananibe pa Mphoto
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 222

Nyimbo 222

Yang’ananibe Maso Anu Pamphotho!

(2 Akorinto 4:18)

1. Pomwe akhungu apenya

Ndipo ogontha amvanso,

Pamene madzi abwino

Adzayenda m’chipululu,

Wopuŵala adzadumpha,

Okondedwa sadzafanso—

Udzawonatu nthaŵiyo,

Poyang’anabe pamphotho.

2. Wosalankhula ’lankhula,

Wokalamba ku’nyamata,

Pomwe dziko litulutsa

Chuma, zabwino nzosatha

Pomveka nyimbo za ana,

Padzakhalatu mtendere,

Ndi akufa adzauka,

Poyang’anabe pamphotho.

3. Mmbulu ndi mwana wankhosa,

Mwana wang’ombe pamodzi,

Mwana adzatsogolera,

Ndipo zonsezidzamvera.

Pamene mantha, misozi,

Ndi kupweteka zichoka,

M’lungu agaŵira zonse,

Poyang’anabe pamphotho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena