Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 180
  • Bukhu la Mulungu—Chuma

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bukhu la Mulungu—Chuma
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Buku la Mulungu Ndi Chuma Chamtengo Wapatali
    Imbirani Yehova
  • Baibulo Ndi Chuma
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 180

Nyimbo 180

Bukhu la Mulungu—Chuma

(Miyambo 2:1)

1. Pali Bukhu, lamasamba ambiri,

Libweretsa mtendere kwa anthu.

Malingaliro ake ngamphamvudi;

Lichititsa ‘akhungu’ kuwona.

Bukhulo ndi Baibulo loyera.

Linalembedwa mouziridwa,

Ndi anthu okonda Yehova M’lungu,

Mzimu wake unawathandiza.

2. Analemba cholembedwa chowona,

Za chilengedwe chake chonsecho.

Anenanso za ungwiro wa munthu

Ndi kutayika kwa Paradaiso.

Anena za mngelo wina amene

Anapandukira Ufumuwo.

Ndi kutsogoza anthu muuchimo,

Koma Yehova adzalakika.

3. Tikhalatu ndi moyo muchimwemwe.

Ufumu wa Mulungu wayamba.

Yehova wapatsa chipulumutso

Kwa onse omadza kwa iye yo.

Mbiriyi timaipeza m’bukhulo;

Simafanananso ndi golidi.

Ipatsa chiyembekezo choposa;

Imaposatu mbiri zonsezo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena