Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 56
  • Pitirizanibe Molimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizanibe Molimba Mtima
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 56

Nyimbo 56

Pitirizanibe Molimba Mtima

(1 Timoteo 1:12)

1. Yemwe ali wokhulupirika,

Sadzakhala ndi mantha,

Achita umboni molimba mtima,

Kuti Ufumu wadza.

(Korasi)

2. Chikhulupiro chisonkhezera;

Chikondi chithandiza.

Changu kwa Mfumu chitikangalitsa;

Ndipo dyera lichoke.

(Korasi)

3. Yehova ndiwamphamvu munkhondo,

Amatilimbikitsa

Mpaka Armagedo iwonongadi

Dongosolo lakale.

(KORASi)

Tiyenitu. Molimbika.

Cho’nadi chitsogoze.

Ati Yehova: “Ndidzakulimbitsa;

Menyera chowonadi.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena