Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 163
  • Chipatso cha Mzimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chipatso cha Mzimu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Woleza Mtima
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mafunso Ochokera Kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Kodi ‘Mupitiriza Kuyenda mwa Mzimu’?
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Kodi Mukulola Mzimu wa Mulungu Kukutsogolerani?
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 163

Nyimbo 163

Chipatso cha Mzimu

(Agalatiya 5:22, 23)

1. Zipatso za mzimu wa M’lungu

Ife tonse titulutse,

Kuti timlemekeze iye,

Adzatipatsatu moyo.

Nthaŵi zonse tisonyezetu

Chikondi chaumulungu

Sangalalani nthaŵi zonse,

Chimwemwe chipatsa mphamvu.

2. Tikhale ndi mtendere wa Ya

Tikhalenso muumodzi.

Kuleza mtima nkofunika,

Kuti tipilire zonse.

Chifundo chidzetsa zabwino!

Chichititsa ena kumva,

Ubwino umatithandiza

Kugaŵana chimwemwecho.

3. Chipatso cha chikhulupiro

Chipatsa nyonga nchifuno.

Kudekha kulidi kwabwino!

Kumathetsa mikangano.

Kudziletsa nkofunikanso,

Kuti tisatayiketu.

Mwa kubala zipatso izi,

Tidzayanjidwa ndi M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena