Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 165
  • Tamandani Ya Limodzi Nane!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Ya Limodzi Nane!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Mwana Wake Wodzozedwa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 165

Nyimbo 165

Tamandani Ya Limodzi Nane!

(Salmo 145:21)

1. Tamani Ya, Mfumu yathu.

Anthu onse amulemekeze.

Tidalitse dzina lake,

Uzani anthu za mphamvu yake.

Inde, nenani za mphamvu yake.

2. Tamani Ya. Wachifundo

Aleza mtima ndi ife tonse.

Wodabwitsa ndi wamkulu;

Zochita zake nzosangalatsa.

Inde, nzosangalatsa kwambiri.

3. Tamani Ya. Mgaŵiriyo

Apatsa chakudya kwa onsewo.

Alimbitsa ofooka.

Bwanji anthu samayamikira?

Inde, anthu ayamikiretu.

4. Tamani Ya, Ngwapafupi;

Kwa onse oitana amvera.

Awononga oipawo,

Adzasunga onse omkondawo.

Inde, adzasunga omkondawo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena