Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 39
  • Gulu Lankhondo la Mulungu Likupita Patsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Gulu Lankhondo la Mulungu Likupita Patsogolo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 39

Nyimbo 39

Gulu Lankhondo la Mulungu Likupita Patsogolo

(1 Timoteo 6:12)

1. Ankhondo a Mulungu;

Alidi amphamvu

Kutamanda Yehova,

Nasunga lamulo.

Ngakhale chinjokacho

Chilimbika nkhondo,

Mthunzi wa dzanja lake

M’lungu atisunga.

2. Njolimba nkhondo yathu

M’tsiku la Yehova.

Tilankhula molimba.

Tiwopsedwerenji?

Mwana wake ndi Ngwazi,

Amenyera bwino.

Ayamba kumenyako;

Tiyeni nayetu.

3. Tipita patsogolo;

M’lungu adzalaka.

Changu chisalephere,

Timlemekezetu!

Chilakiko chidzadi,

Mphotho yalonjezo

Idikira amphumphu,

Osatula chida.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena