Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 26
  • Kukwaniritsa Zofunika za Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukwaniritsa Zofunika za Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Zisangalalo ndi Zipatso za Utumiki Waufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kukhala ndi Moyo Mogwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • O Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mulungu Wamkulu, Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 26

Nyimbo 26

Kukwaniritsa Zofunika za Mulungu

(Chivumbulutso 12:17)

1. Tidalirike kwa M’lungu,

Tiri kusunga umphumphu.

Kunyumba ndi nyumba timke

Kulalika za Yehova.

Monga Mboni ife timka

Kuŵatonthoza olira;

Kulemba pamphumi pawo,

Kuti apulumutsidwe.

2. Ngati tidzipenyerera,

Tidzaŵala mokwanira.

Moyo wosatha ndiwathu,

Poutchinjiriza mtima.

Ife tikalalikira,

Ambiri adzamva Mawu.

Powongola njira zathu,

Chimwemwe chidzakwanira.

3. Tithandizetu abale,

Ndiponso anansi athu,

Ndikukhala mumtendere,

Ndi otumikira M’lungu.

Tiyamikira kwambiri,

Gawo lakutumikira.

Mosalakwa tilisunge,

Kulemekeza Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena