Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 136
  • Olambira Okhulupirika Alemekeza Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Olambira Okhulupirika Alemekeza Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Okhulupirika Anu Adzakulemekezani
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 136

Nyimbo 136

Olambira Okhulupirika Alemekeza Yehova

(Salmo 18:25)

1. Okhulupirika, akutamandani;

Chotero, dzetsani chipambano.

Tikutamandeni; Muli wolungama.

Timachita ntchito mowonadi.

2. Tilemekeza’nu—tikuthokozani—

Tisamale zonse, ndi chiyero.

Chonde tidziŵetu chikhulupiliro.

Mbuye tisonyeze umphumphuwo.

3. Tidziŵitseni za Ufumu wanuwo

Mumachirikiza mwapamwamba.

Sonyani ubwino, kuti asagwedi.

Mutimve kupempha, mosaleka.

4. Tate m’tithandize, kugonjetsa mantha,

Ponena Ufumu titamenu.

Mtendere wambiri, pokutamandani

Mudziko lonseli, titamanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena