Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 111
  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwala Kukuwonjezerekabe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuwala Kukuwonjezereka
    Imbirani Yehova
  • Tsatirani Kuunika kwa Dziko
    Nsanja ya Olonda—1993
  • “Kuunika Kunadza ku Dziko Lapansi”
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 111

Nyimbo 111

Kuunika Kumkabe Kuuŵala

(Miyambo 4:18)

1. Kuunika kwa Mawu kuŵalabe,

Ku kuŵalirirabe Tsikulo lidza (mwamsangaditu).

Cho’nadi cha Ufumu chiwoneka;

Kwa ife akupempha: ‘Mvetseranitu’ (kwambiridi).

Nthaŵi yapita pamene

Tinaikidwa mundende.

Tsiku Lake.

Cho’nadi chadza.

Kuŵala kuwoneka ngati dzuŵa,

Kuunika kuŵalira olungamawo,

Kuŵala kwa Ya.

2. Kuŵala panjira ya olungama.

Yehova achititsa Mwachikondidi (chachikuludi).

Avumbula kumvetsetsa kowona;

Aumba anthu ake ndi chowonadi (cha ufumu).

Chifukwa chosalungama

Pangakhale kupatuka;

Chowonadi

Chikuŵalabe.

Mulungu watumiza chithandizo.

Aunikira mwaulemelero wake,

Kuŵalirabe.

3. Kuŵalako ku’nikira panjira

Monga dzuŵa masana kopanda mtambo (kokongoladi).

Ya nkuŵala amatiunikira;

Aŵalitsa njirayo, tisausetu (moyo wathu).

Tisakayikire ndithu,

Kukakamiza cho’nadi.

Munjirayo

Tikhalemobe.

Kuŵala kudzawonjezerekabe.

Olungama akondwera nako kuŵala.

Kuunikadi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena