Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 40
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 40

Nyimbo 40

Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba

Losindikizidwa

(Mateyo 6:33)

1. Chomwe Yehova afuna,

Chomwe chim’sangalatsa,

Ndicho Ufumu wa Khristu,

Womwe ukonze zonse.

(KOLASI)

M’fune Ufumu choyamba

Ndi chilungamo chake.

M’tamande pa amitundu

Ndi kum’tumikirabe.

2. Musade nkhawa n’zamawa

Za chakudya ndi madzi.

M’lungu atisamalira

Tikafuna Ufumu.

(KOLASI)

M’fune Ufumu choyamba

Ndi chilungamo chake.

M’tamande pa amitundu

Ndi kum’tumikirabe.

3. Tsono lalika uthenga

Uthandize enanso

Azidalira Yehova

Ndi Ufumu wakewo.

(KOLASI)

M’fune Ufumu choyamba

Ndi chilungamo chake.

M’tamande pa amitundu

Ndi kum’tumikirabe.

(Onaninso Sal. 27:14; Mat. 6:34; 10:11, 13; 1 Pet. 1:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena