Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 49
  • Yehova Ndi Pothawira Pathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Pothawira Pathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Ndi Pothawirapo Pathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Ndiye Pothaŵirapo Pathu
    Nsanja ya Olonda—2001
  • ‘Pezani Chitetezo M’dzina la Yehova’
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 49

Nyimbo 49

Yehova Ndi Pothawira Pathu

Losindikizidwa

(Salmo 91)

1. Yehova m’pothawira

Tidalira iye.

Tikhalebe mumthunzi

Wake, tisachoke.

Iye adzatiteteza,

Tidalire mphamvu zake.

Yehova M’lungu wathu,

Ateteza olungama.

2. Kaya ambiri agwe

Pambali pa iwe,

Udzatetezeka ndi

Okhulupirika.

Sudzaopa ngati kuti

Ndiwe udzawonongedwe

Udzaziona izi,

Uli mumapiko ake.

3. M’lungu akuteteza

Ukamayesedwa.

Sudzafooka ayi

Chifukwa cha mantha.

Sudzaopa mkango, ndipo

Chinjokanso udzaponda.

Yehova m’pothawira,

Amatisamaliradi.

(Onaninso Sal. 97:10; 121:3, 5; Yes. 52:12.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena