Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 36
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Anthu Achimwemwe a Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 36

Nyimbo 36

“Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Losindikizidwa

(Mateyo 19:5, 6)

1. Mulungu ndi anthu

Amva malonjezo.

Chingwe cholimba bwino

Chamangidwa lero.

Awa alonjezana

Kuti akondane.

(KOLASI)

‘Chomwe M’lungu wamanga

Musalekanitse.’

2. Cholinga cha M’lungu

Anachifufuza.

Kupeza madalitso

N’komwe akufuna.

Awa agwirizana

Kuti akondane.

(KOLASI)

‘Chomwe M’lungu wamanga

Musalekanitse.’

(Onaninso Gen. 2:24; Mla. 4:12; Aef. 5:22-33.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena