Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 63
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Kodi Mumasangalala ndi Chikondi Chokhulupirika Ngati Mmene Yehova Amachitira?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Chikondi Chokhulupirika cha Yehova N’chachikulu
    Nsanja ya Olonda—2004
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 63

Nyimbo 63

Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse

Losindikizidwa

(Salimo 18:25)

1. Tikhulupirike zedi

Kwa M’lungu ndi kum’konda.

Kuphunzira malamulo

Ake tifunikira.

Sangatigwiritse mwala

Tikamamvera Iye.

Ndi wokhulupirikadi

Ndipo sitingam’siye.

2. Tikhulupirike zedi

Kwa ’bale pamavuto,

Tikhale okoma mtima

M’mawu ndiponso m’ntchito.

Tilemekeze abale,

Tiwakhulupirire.

Baibulo litigwirizanitse

Nthawi zonse.

3. Tikhulupirike zedi

Tikamalangizidwa,

Ndi abale amumpingo,

Tifunika kumvera.

Tidzapeza madalitso

Ochoka kwa Yehova.

Tikakhulupirikadi

Iye adzatikonda.

(Onaninso Sal. 149:1; 1 Tim. 2:8; Aheb. 13:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena