Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 108
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Mwana Wake Wodzozedwa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tipita Nanu Limodzi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 108

Nyimbo 108

Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 21:2)

1. Yehova ’nadzoza Yesu

Kuti alamulire,

Kuti chifuniro cha M’lungu

Padzikoli chichitike.

(KOLASI)

Tamandani Yehova ndithu

Chifukwa cha Wodzozedwa

Inu nkhosa zokhulupirika

Zomvera malamulo.

Tamandani Wodzozedwayo,

Wolamula wakumwamba,

Amene adzayeretsa dzina

Loyera la Mulungu.

2. Abale a Yesu Khristu

Iwo ndi osankhika.

Adzalamulira ndi Yesu.

Dzikoli adzayeretsa.

(KOLASI)

Tamandani Yehova ndithu

Chifukwa cha Wodzozedwa

Inu nkhosa zokhulupirika

Zomvera malamulo.

Tamandani Wodzozedwayo,

Wolamula wakumwamba,

Amene adzayeretsa dzina

Loyera la Mulungu.

(Onaninso Miy. 29:4; Yes. 66:7, 8; Yoh. 10:4; Chiv. 5:9, 10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena