Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 124
  • Alandireni Bwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Alandireni Bwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Alandireni Bwino
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Cherezani Alendo’
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kuchereza Alendo Ndi Kofunika Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tizichitira Ena “Zabwino” Pokhala Ochereza (Mat. 12:35a)
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 124

Nyimbo 124

Alandireni Bwino

Losindikizidwa

(Machitidwe 17:7)

1. Yehova ndi M’lungu wopanda tsankho

Amapatsa onse zofuna zawo.

Amapatsa dzuwa

Ngakhalenso mvula

Amatisangalatsa mtima.

Osauka tikamawathandiza.

Mulungu wathu tidzamutsanzira,

Adzatidalitsa tikamachitira

Ena zinthu mokoma mtima.

2. Pothandiza ena sitingadziwe

Madalitso omwe tingalandire.

Angakhale anthu achilendo ndithu,

Tiwapatse zosowa zawo.

Monga Lidiya wa m’nthawi yakale,

Akabwera kwathu tiwalandire.

M’lungu amadziwa

onse om’tsanzira

Pochitira ena chifundo.

(Onaninso Mac. 16:14, 15; Aroma 12:13; 1 Tim. 3:2; Aheb. 13:2; 1 Pet. 4:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena