Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 73
  • Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Koposa Zonse Mukhale Nacho Chikondano Chenicheni”
    Dikirani!
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 73

Nyimbo 73

Tizikondana Kwambiri Kuchokera Mumtima

Losindikizidwa

(1 Petulo 1:22)

1. Tiyenera kukondana

Mochokeradi mumtima

Zimene zimapangitsa

Kuti tizikondwa.

Chikondi chili mumtima

Tifuna kuchisonyeza

Potero tidzatsanzira

Atate Yehova.

Mawu ndi ntchito zathu

Zisonyeze kukonda ’nzathu.

Osowa tithandize

N’zomwe tingakwanitse.

Tichitire’na ulemu

Pamene athedwa nzeru,

Ayi tisawanenetu.

Tidzakhulupirika,

Tidzagwirizanika.

2. Pamenetu tikondana

Sitikwiyirana msanga,

Tikhala osangalala,

Ndi kudalirana.

Tidzakhala ndi mabwenzi

Omwe tingadaliredi,

Ndi kumakondana zedi

Ndi kumasonkhana.

Tonse timalakwitsa

N’kulankhula mosaganiza,

Choncho ndikofunika

Chifundo kusonyeza.

Timafuna kudziwika

Monga anthu okondana.

Choncho M’lungu wakumwamba

Tidzamulemekeza,

Inde kumutsanzira.

(Onaninso 1 Pet. 2:17; 3:8; 4:8; 1 Yoh. 3:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena