Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 131
  • Yehova Amapereka Chipulumutso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amapereka Chipulumutso
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amapereka Populumukira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova, Wopereka Populumukira
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 131

Nyimbo 131

Yehova Amapereka Chipulumutso

Losindikizidwa

(2 Samueli 22:1-8)

1. Yehova ndinu M’lungu wamphamvuyonse.

Timaona izi m’chilengedwe chonse.

Kulibe m’lungu wina angachite zimene

Inu mumachita.

(KOLASI)

Yehova amapatsa pothawira.

Tidzaonadi kuti iye ndi Thanthwe.

Choterotu tilengezebe za Yehova

Mpulumutsi wathu. Titero mosaopa.

2. Ngakhale zingwe za imfa zandizinga

Ndikupempha kuti ndilimbedi mtima.

Mumve pemphero langa: “Nditetezeni chonde,

Ndipulumutseni.”

(KOLASI)

Yehova amapatsa pothawira.

Tidzaonadi kuti iye ndi Thanthwe.

Choterotu tilengezebe za Yehova

Mpulumutsi wathu. Titero mosaopa.

3. Mawu anu onga bingu adzamveka.

Olimbana nanu adzanjenjemera.

Mudzakhala chimene mukufuna kukhala.

Onse adzaona.

(KOLASI)

Yehova amapatsa pothawira.

Tidzaonadi kuti iye ndi Thanthwe.

Choterotu tilengezebe za Yehova

Mpulumutsi wathu. Titero mosaopa.

(Onaninso Sal. 18:1, 2; 144:1, 2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena