Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 133
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 133

Nyimbo 133

Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke

Losindikizidwa

(Zefaniya 2:3)

1. Mitundu ya anthu

Ikutsutsadi Yesu.

Nthawi yawo yolamula

Yatha watero M’lungu.

Ufumu wayamba

Ndipo wakhazikika.

Adani onse apadziko

Khristu adzawaphwanya.

(KOLASI)

Bweranitu kwa Yehova

Kuti mudzapulumuke.

Mumudalire,

M’khulupirike,

Khalani kumbali yake.

Adzakupulumutsani

Ndi mphamvu zake.

2. Sankhani tsopano

Anthunu apadziko

Kumvera kaya kukana

Uthengawu wabwino.

Ngakhale mavuto

Tingakumane nawo

Yehova amasamalira

Tikapempha thandizo.

(KOLASI)

Bweranitu kwa Yehova

Kuti mudzapulumuke.

Mumudalire,

M’khulupirike,

Khalani kumbali yake.

Adzakupulumutsani

Ndi mphamvu zake.

(Onaninso 1 Sam. 2:9; Sal. 2:2, 3, 9; Miy. 2:8; Mat. 6:33.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena