Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 38
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Umutulire Yehova Nkhawa Zako
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Umsenze Yehova Nkhaŵa Zako
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 38

Nyimbo 38

Umutulire Yehova Nkhawa Zako

Losindikizidwa

(Salmo 55)

1. Chonde, ndimveni Yehova,

Musandinyalanyaze.

Mundiyankhe pempho langa,

Mundichotsere mantha.

(KOLASI)

Tulira Yehova nkhawa

Ndipo adzakuchirikiza.

Iye sadzalola kuti

Ugwedezeke konse.

2. N’kadakhala ndi mapiko,

Ndikanaulukadi,

Kuti ofuna kundipha,

Asandipeze konse.

(KOLASI)

Tulira Yehova nkhawa

Ndipo adzakuchirikiza.

Iye sadzalola kuti

Ugwedezeke konse.

3. Ndidzafu’lira Yehova

Kuti anditeteze.

Iye apatsa mtendere Kwa

atumiki ake.

(KOLASI)

Tulira Yehova nkhawa

Ndipo adzakuchirikiza.

Iye sadzalola kuti

Ugwedezeke konse.

(Onaninso Sal. 22:5; 31:2-24.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena