Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 134
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 134

Nyimbo 134

Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 21:1-5)

1. Yerekeza iwe ndi’ne

M’dziko la tsopano tili tonse.

Ona mmene udzamvere,

Kukhala m’dziko la mtendere.

Oipa onse achoka.

M’lungu wathu sadzalephera

Kusintha zonse padziko lapansi.

Tidzamuimbira nyimbo tikumati:

(KOLASI)

“Yehova M’lungu mwachita bwino,

Zonse zakhalano zatsopano.

Tikuimba nyimbo mwachisangalalo.

Ndinudi woyenera ulemelero.”

2. Taganizira m’tsogolo,

Iwe ndi’ne m’dziko latsopano.

Sitidzamva ndi kuona

Zinthu zotichititsa mantha.

Mmene analonjezera

Zachitika, zonse zatheka.

Tsopano aku’kitsa omwalira,

Iwo ndi ife tidzamuyamikira:

(KOLASI)

“Yehova M’lungu mwachita bwino,

Zonse zakhalano zatsopano.

Tikuimba nyimbo mwachisangalalo.

Ndinudi woyenera ulemelero.”

(Onaninso Sal. 37:10, 11; Yes. 65:17; Yoh. 5:28; 2 Pet. 3:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena