Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 42
  • “Muthandize Ofookawo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Muthandize Ofookawo”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Muzithandiza Ofooka”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Muyenera Kuthandiza Ofookawo’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Kondanani Wina ndi Mnzake’
    Nsanja ya Olonda—2003
  • “Pamene Ndili Wofooka, M’pamene Ndimakhala Wamphamvu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 42

Nyimbo 42

“Muthandize Ofookawo”

Losindikizidwa

(Machitidwe 20:35)

1. Tonse tili n’zofo’ka

Pamoyo wathu.

Komabetu Yehova

Amatikonda.

Iye n’ngwachifundo,

Atisamalira.

Tisonyeze chikondi

Kwa ovutika.

2. Kodi ndani safo’ka

Panthawi zina?

Khristu anatigula,

Tipeze moyo.

Ofo’ka n’nga M’lungu,

Awalimbikitsa.

Timve zovuta zawo

Tiwatonthoze.

3. Tisanyoze ofo’ka,

Tiwakumbuke

Inde, tiwasonyeze

Kukoma mtima.

Tichitedi khama,

Powalimbikitsa.

Tikawathandizadi

Atonthozedwa.

(Onaninso 2 Akor. 11:29; Yes. 35:3, 4; Agal. 6:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena