Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 7
  • Tidzipereke Monga Akhristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tidzipereke Monga Akhristu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Kudzipereka Monga Mkhristu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kudzipatulira Kwachikristu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Odzipatulira—Kwa Yani?
    Nsanja ya Olonda—1995
  • N’chifukwa Chiyani Muyenera Kudzipereka kwa Yehova?
    Nsanja ya Olonda—2010
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 7

Nyimbo 7

Tidzipereke Monga Akhristu

Losindikizidwa

(Aheberi 10:7, 9)

1. Yehova analengatu

Chilengedwe chonse,

Dzikoli ndi mlengalenga

Zonsezi ndi zake.

M’lungu watipatsa moyo

Wasonyeza kuti

Ndi woyenera kum’tamanda

Ndiponso kum’lambira.

2. Yesu anabatizidwa

Nanena m’pemphero:

‘Ndabwera kuti ndichite

Chifuniro chanu.’

Anatuluka m’Yo’dano

Monga wodzozedwa,

Kuti atumikire M’lungu

Monga wodzipereka.

3. Yehova, ife tabwera

Kukutamandani.

Tadzipereka kwa inu

Ndipo tadzikana.

Munapereka Mwana’nu,

Nalipira dipo.

Tasiyatu zofuna zathu,

Tizichitano zanu.

(Onaninso Mat. 16:24; Maliko 8:34; Luka 9:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena