Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 111
  • Iye Adzaitana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Iye Adzaitana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Iye Adzaitana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 111

Nyimbo 111

Iye Adzaitana

Losindikizidwa

(Yobu 14:13-15)

1. Moyo wathu uli ngati nkhungu,

Mwamsanga umapita.

Mu kanthawi kochepa kwambiri

Tingayambe kulira.

Kodi akufa angadzukenso?

M’lungu akulonjeza:

(KOLASI)

Iye adzawaitana

Akufa adzayankha.

Ntchito yamanja ake

Adzailakalaka.

Choncho khulupirirani

M’lungu adzatidzutsa

Mongadi anthu ake.

Tidzakhala kosatha.

2. Anthu a M’lungu angamwalire

Koma saiwalidwa.

Omwe M’lungu akukumbukira

Onse adzadzutsidwa.

Ndipo ife tidzasangalala

Ndi moyo wamuyaya.

(KOLASI)

Iye adzawaitana

Akufa adzayankha.

Ntchito yamanja ake

Adzailakalaka.

Choncho khulupirirani

M’lungu adzatidzutsa

Mongadi anthu ake.

Tidzakhala kosatha.

(Onaninso Yoh. 6:40; 11:11, 43; Yak. 4:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena