Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 88
  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Muzikhulupirira Abale Anu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kukhulupirira Ena N’kofunika Kwambiri Kuti Munthu Akhale Wosangalala
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Abusa Ndi Mphatso
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 88

Nyimbo 88

Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 127:3-5)

1. Mwamuna ’kakhala bambo,

Mkazinso akakhala ndi mwana.

Afunika akumbukire,

Mwanayo siwawo okha.

Ndi mphatso yochoka kwa M’lungu

Amapatsa chikondi ndi moyo.

Amapatsanso malangizo

Othandizadi kwa makolo.

(KOLASI)

Mphatso yanu njopatulika

Ndipo muisamalire.

M’phunzitseni mwana cho’nadi

Choncho mungamuthandize.

2. Malamulo ’nse a M’lungu

Muziwasunga mumtima mwanu.

Muziphunzitsa ana anu,

Uwu ndi udindo wanu.

Muziwaphunzitsa poyenda,

Podzuka ndi pa nthawi yopuma.

Choncho iwo sadzaiwala

Adzakhala odalitsidwa.

(KOLASI)

Mphatso yanu njopatulika

Ndipo muisamalire.

M’phunzitseni mwana cho’nadi

Choncho mungamuthandize.

(Onaninso Deut. 6:6, 7; Aef. 6:4; 1 Tim. 4:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena