Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 77
  • Muzikhululuka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikhululuka
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhululuka
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani Wokhululukira
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Pitirizani Kukhululukirana Eni Okha’
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Khululukani Kuchokera Mumtima
    Nsanja ya Olonda—1999
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 77

Nyimbo 77

Muzikhululuka

Losindikizidwa

(Salimo 86:5)

1. Mwachikondi M’lungu

Mwa Yesu anakonza

Kuti tikhululukidwe

Ndi kuthetsadi imfa.

Ngati tilidi olapa,

Ndipo titamupempha,

Pogwiritsa ntchito

Dipo Atikhululukira.

2. Ngati titsanzira

Mulungu wakumwamba

Kukhululukira ena

Tidzakhululukidwa.

Tikhale ololerana,

Tisakhale odana

Koma olemekezana

Komanso okondana.

3. Tikhale n’chifundo,

Chidzatithandizadi

Kusasunga chakukhosi

Kapenanso chidani.

Tikatsanzira Yehova

Maka chikondi chake

Tidzakhululukirana

Tidzafanana naye.

(Onaninso Mat. 6:12; Aef. 4:32; Akol. 3:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena