Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 37
  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Malemba—Ouziridwa ndi Opindulitsa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Malemba Anauziridwa Ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mawu a Mulungu Azikuthandizani Ndipo Muzithandiza Nawo Ena
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Musalole Kuti Chilichonse Chikulepheretseni Kulandira Mphoto
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 37

Nyimbo 37

Malemba Anauziridwa ndi Mulungu

Losindikizidwa

(2 Timoteyo 3:16, 17)

1. M’dzikoli, Mawu a M’lungu

Amatiunikira.

Tikawatsatira bwino,

Cho’nadi chitimasula.

2. Mawu ndi ouziridwa,

Amatiphunzitsadi.

Amawongoladi zinthu

Ndiponso kutilangiza.

3. Malemba akumwambawa,

Atidziwitsa M’lungu.

Ngati timawawerenga,

Tingadzapezedi mphoto.

(Onaninso Sal. 119:105; Miy. 4:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena