Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 114
  • Buku la Mulungu Ndi Chuma Chamtengo Wapatali

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Buku la Mulungu Ndi Chuma Chamtengo Wapatali
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Baibulo Ndi Chuma
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Bukhu la Mulungu—Chuma
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 114

Nyimbo 114

Buku la Mulungu Ndi Chuma Chamtengo Wapatali

Losindikizidwa

(Miyambo 2:1)

1. Pali buku limene mawu ake

Amatibweretsera chimwemwe.

Mfundo zake zodabwitsa n’zamphamvu,

Zimathandiza ’khungu aone.

Bukuli ndi Baibulo loyera.

Olilemba anauziridwa,

Ankakonda Yehova M’lungu wawo.

Mzimu wake unawathandiza.

2. Analemba zokhudza chilengedwe.

Mmene M’lungu anachilengera.

Analembanso za Paradaiso

Ndiponsotu mmene anathera.

Analemba za mngelo winawake

Amene ananyoza Yehova.

Zinabweretsa chisoni pa anthu

Koma Yehova adzapambana.

3. Masiku ano tili ndi chimwemwe,

Ufumu wa Mulungu wayamba.

Yehova ’kupatsa chipulumutso

Kwa onse omwe amamukonda.

M’buku lake muli zosangalatsa,

Chakudya chamwanaalirenji.

Limatipatsa mtendere wambiri,

N’lofunika kuliwerengadi.

(Onaninso 2 Tim. 3:16; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena