Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 96
  • Fufuzani Anthu Oyenerera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fufuzani Anthu Oyenerera
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Fufuzani Anthu Oyenerera
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Mulungu Wamkulu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 96

Nyimbo 96

Fufuzani Anthu Oyenerera

Losindikizidwa

(Mateyu 10:11-15)

1. Ambuye wathu anatisonyeza

Njira yolalikirira:

‘Kulikonse kumene mungapite

Fufuzani oyenerera.

Muziwapatsa moni eni nyumba

Ndikuwafunira mtendere.

Ngati akana sansani fumbi

Kumapazi anu muwasiye.’

2. Onse amene akulandirani

Alandiranso Ambuye.

Mulungu adzawathandizadi

Kuti nawonso atumikire.

Musade nkhawa kuti munenanji,

Yehova adzakuuzani.

Ngati mutayankha mokoma mtima

Ofatsa adzakumverani.

(Onaninso Mac. 13:48; 16:14; Akol. 4:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena