Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 57
  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Zimene Ndimaganizira Mozama”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kusinkhasinkha Kumene Kumapindulitsa
    Galamukani!—2000
  • Kusinkhasinkha
    Galamukani!—2014
  • Tiziganizira Kwambiri za Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 57

Nyimbo 57

Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga

Losindikizidwa

(Salimo 19:14)

1. Zomwe ndimasinkhasinkha,

Zimene ndimaganiza,

Zikukondweretseni Ya

Kuti ndikhale wolimba.

Pamene ndili ndi nkhawa

N’kumalephera kugona

Ndisinkhesinkhe za inu,

Inde zinthu zoyenera.

2. Zilizonse zolungama,

Zofunika ndi zoona,

Ndikamaziganizira

Zindipezetse mtendere.

Nzeru zanu n’zofunika

Komanso ndi zochuluka.

Choncho ndizisinkhasinkha

Zonena zanu mwakhama.

(Onaninso Sal. 49:3; 63:6; 139:17, 23; Afil. 4:7, 8; 1 Tim. 4:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena