Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 30
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Iri Nditsiku la Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muziika Ufumu Pamalo Oyamba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitirizani Kufuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 30

Nyimbo 30

Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 11:15)

1. Tsikuli n’lapadera. M’lungu akulamula.

Waikatu mwala mu Ziyoni.

Onse akweze mawu. Aimbire Mulungu.

Khristu Mpulumutsi wakhala pampando.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

2. Khristu ali pampando, Nkhondo yayandikira.

Dongosolo la Satana litha.

Ndi nthawi yolalika kwa anthu ochuluka.

Nyengo yoti ofatsa asankhe M’lungu.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

3. Tidalira Mfumuyo. Ndi yochititsa chidwi.

Ibwera mu dzina la Yehova.

Tilowe mukachisi, Tim’pembedze Mulungu.

Posachedwa adzalamulira zonse.

(KOLASI)

Kodi Ufumu wa Yehova

Udzabweretsa chiyani?

Udzadzetsa moyo wosatha

Ndi chimwemwe chochuluka.

Tamanda Mfumu yosatha

Iye ndi wachifundo.

(Onaninso 2 Sam. 7:22; Dan. 2:44; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena