Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 115
  • Khalani ndi Moyo Wopambana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani ndi Moyo Wopambana
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 115

Nyimbo 115

Khalani ndi Moyo Wopambana

Losindikizidwa

(Yoswa 1:8)

1. Mawu a Yehova M’lungu

Tiwerenge tonse

Ndipo tiwasinkhesinkhe

Tsiku lililonse.

Iwo atitsogolere

M’zomwe timachita,

(KOLASI)

Ukawerenga n’kumvera

Udzadalitsidwa.

Yenda ndi M’lungu upeze

Njira yopambana.

2. Mafumu mu Is’raeli

Analamulidwa:

‘Chilamulo cha Mulungu

Adzilemberetu.

Ndipo tsiku lililonse

Azichiwerenga.’

(KOLASI)

Ukawerenga n’kumvera

Udzadalitsidwa.

Yenda ndi M’lungu upeze

Njira yopambana.

3. Tikamaphunzira Mawu

Tsiku lililonse

Tikhala n’chiyembekezo

Komanso mtendere.

Tidzapita patsogolo

Tikasinkhasinkha.

(KOLASI)

Ukawerenga n’kumvera

Udzadalitsidwa.

Yenda ndi M’lungu upeze

Njira yopambana.

(Onaninso Deut. 17:18; 1 Maf. 2:3, 4; Sal. 119:1; Yer. 7:23.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena