Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 8
  • Kuwala M’dziko Lamdima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwala M’dziko Lamdima
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwala M’dziko Lamdima
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuunika kwa Mulungu Kumachotsa Mdima!
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 8

Nyimbo 143

Kuwala M’dziko Lamdima

(2 Akorinto 4:6)

  1. M’dzikoli mulitu mdima,

    Anthu sakumvera.

    Koma taona kuwala,

    Ngati m’bandakucha.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu,

    Wawala ngati dzuwa

    M’dziko lamdimali.

    Ukupatsa anthu

    Onse chiyembekezo

    Mdima watha.

  2. Tidzutse omwe agona,

    Poti nthawi yatha.

    Ndipo tiwalimbikitse,

    Tiwapempherere.

    (KOLASI)

    Uthenga wa M’lungu,

    Wawala ngati dzuwa

    M’dziko lamdimali.

    Ukupatsa anthu

    Onse chiyembekezo

    Mdima watha.

(Onaninso Yoh. 3:19; 8:12; Aroma 13:​11, 12; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena