Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 137
  • Akazi Achikhristu Okhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Akazi Achikhristu Okhulupirika
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Akazi Okhulupirika Ndiponso Alongo Achikhristu
    Imbirani Yehova
  • Muzilimbikitsa Alongo Mumpingo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Kodi Mumaona Akazi Ngati Mmene Yehova Amawaonera?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • ‘Akazi Amene Agwiritsa Ntchito mwa Ambuye’
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 137

NYIMBO 137

Akazi Achikhristu Okhulupirika

Losindikizidwa

(Aroma 16:2)

  1. 1. Sara, Esitere, Rute ndi ena,

    Iwo anali akazi abwino.

    Anali odzipereka kwa M’lungu.

    Timawadziwa ndi mayina awo.

    Panali ena sanatchulidwe

    Nawonso Yehova ankawakondanso.

  2. 2. Akaziwatu amatikumbutsa

    Makhalidwe omwe tizisonyeza

    Monga ubwino ndi kulimba mtima.

    Zitsanzo zawo n’zotilimbikitsa.

    Alongo a masiku anonso

    Khalani zitsanzo kwa ena tonsefe.

  3. 3. Amasiye, achemwali, amayi,

    Mumachita khama pogwira ntchito.

    Mumagonjera, mumadzichepetsa.

    Musaope Mulungu ali nanu

    Ndipo iye akulimbitseni.

    Mukhulupirike, mudzadalitsidwa.

(Onaninso Afil. 4:3; 1 Tim. 2:​9, 10; 1 Pet. 3:​4, 5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena