Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 66
  • Lengezani Uthenga Wabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lengezani Uthenga Wabwino
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Lalikirani Uthenga Wabwino
    Imbirani Yehova
  • Lengezani Mbiri Yabwino Yosatha
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chuma Chapadera
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 66

NYIMBO 66

Lengezani Uthenga Wabwino

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 14:​6, 7)

  1. 1. Poyamba sitinkadziwa za Ufumu.

    Pano tadziwa

    Mfumu yolonjezedwa.

    Mwa chifundo ndi chikondi cha Yehova

    Anaganizira anthu ochimwafe.

    Anakonza zoti pakhale Ufumu

    Ndipo wolamulira waketu ndi Yesu.

    Anakonzanso za kagulu ka nkhosa

    Kodzakhala mkwatibwi wa Mwana wake.

  2. 2. Uthenga wabwinowu tisaubise,

    M’lungu akufuna anthu audziwe.

    Angelo amatithandiza kwambiri

    Pogwira ntchito

    yolengeza Ufumu.

    Tapatsidwa udindo ndiponso mwayi

    Wom’tamanda ndi kuyeretsa dzina lake.

    Tikwaniritse udindo umenewu

    Mwa kulalikira uthenga wabwino.

(Onaninso Maliko 4:11; Mac 5:31; 1 Akor. 2:​1, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena