Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 98
  • Malemba Anauziridwa Ndi Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malemba Anauziridwa Ndi Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Malemba—Ouziridwa ndi Opindulitsa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 98

NYIMBO 98

Malemba Anauziridwa Ndi Mulungu

Losindikizidwa

(2 Timoteyo 3:​16, 17)

  1. 1. Mawu a M’lungu ndi nyale,

    Amatiunikira.

    Tikawagwiritsa ntchito

    Tizikonda choonadi.

  2. 2. Mawu ouziridwawa

    Amatiphunzitsadi.

    Amatha kukonza zinthu

    Ndiponso kutilangiza.

  3. 3. Mawu a Mulungu wathu

    Amatitsogolera.

    Ngati timawawerenga

    Zizitiyendera bwino.

(Onaninso Sal. 119:105; Miy. 4:​13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena